Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 17:26 - Buku Lopatulika

Tsiku lomwelo anadulidwa Abrahamu ndi Ismaele mwana wake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Tsiku lomwelo anadulidwa Abrahamu ndi Ismaele mwana wake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pa tsiku limeneli Abrahamu ndi mwana wake Ismaele adaumbalidwa,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Onse, Abrahamu ndi mwana wake Ismaeli, anachita mdulidwe tsiku limodzi.

Onani mutuwo



Genesis 17:26
5 Mawu Ofanana  

Ndipo anamuka Abramu monga Yehova ananena kwa iye, ndipo Loti anamuka pamodzi naye: ndipo Abramu anali wa zaka makumi asanu ndi awiri kudza zisanu, pamene anatuluka mu Harani.


Ndipo Ismaele mwana wake anali wa zaka khumi ndi zitatu pamene anadulidwa m'khungu lake.


Ndipo amuna onse a m'nyumba mwake obadwa m'nyumba, ndi ogulidwa ndi ndalama kwa alendo, anadulidwa pamodzi naye.


Ndinafulumira, osachedwa, kusamalira malamulo anu.