Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 17:25 - Buku Lopatulika

Ndipo Ismaele mwana wake anali wa zaka khumi ndi zitatu pamene anadulidwa m'khungu lake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Ismaele mwana wake anali wa zaka khumi ndi zitatu pamene anadulidwa m'khungu lake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mwana wake Ismaele anali wa zaka 13 pamene adaumbalidwa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ndipo mwana wake Ismaeli anali ndi zaka khumi ndi zitatu;

Onani mutuwo



Genesis 17:25
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Hagara anambalira Abramu mwana wamwamuna ndipo Abramu anatcha dzina la mwana wake amene anambalira iye Hagara, Ismaele.


Ndipo Abramu anali wa zaka makumi asanu ndi atatu kudza zisanu ndi chimodzi, pamene Hagara anambalira Abramu Ismaele.


Tsiku lomwelo anadulidwa Abrahamu ndi Ismaele mwana wake.