Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 17:22 - Buku Lopatulika

Ndipo analeka kunena naye, ndipo Mulungu anakwera kuchokera kwa Abrahamu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo analeka kunena naye, ndipo Mulungu anakwera kuchokera kwa Abrahamu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mulungu atatha kulankhula ndi Abrahamu, adamsiya pomwepo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atatha kuyankhula, Mulungu anamuchokera Abrahamu.

Onani mutuwo



Genesis 17:22
11 Mawu Ofanana  

Ndipo Abramu anagwa nkhope pansi, ndipo Mulungu ananena naye kuti,


Ndipo Yehova anapita atatha kunena naye Abrahamu: ndipo Abrahamu anabwera kumalo kwake.


Ndipo Yehova anati kwa Mose, Uzitero ndi ana a Israele, kuti, Mwapenya nokha kuti ndalankhula nanu, kuchokera kumwamba.


Pamenepo Yehova anawapsera mtima iwo; nawachokera Iye.


Kulibe munthu anaona Mulungu nthawi zonse; Mwana wobadwa yekha wakukhala pa chifuwa cha Atate, Iyeyu anafotokozera.


Ine ndi Atate ndife amodzi.


Yehova ananena ndi inu popenyana maso m'phirimo, ali pakati pa moto,


Pakuti kunali, pakukwera lawi la moto paguwa la nsembe kumwamba, mthenga wa Yehova anakwera m'lawi la paguwalo; ndi Manowa ndi mkazi wake ali chipenyere; nagwa iwowa nkhope zao pansi.


Pamenepo mthenga wa Yehova anatambasula nsonga ya ndodo inali m'dzanja lake, nakhudza nyamayi ndi mikate yopanda chotupitsa; ndipo unatuluka moto m'thanthwe nunyeketsa nyama ndi mikate yopanda chotupitsa; ndi mthenga wa Yehova anakanganuka pamaso pake.