Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 15:20 - Buku Lopatulika

ndi Ahiti, ndi Aperizi, ndi Arefaimu,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi Ahiti, ndi Aperizi, ndi Arefaimu,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

la Ahiti, la Aperizi, la Arefaimu,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ahiti, Aperezi, Arefaimu,

Onani mutuwo



Genesis 15:20
9 Mawu Ofanana  

Ndipo panali ndeu, abusa a Abramu kudana ndi abusa a Loti. Akanani ndi Aperizi ndipo analinkukhala nthawi yomweyo m'dzikomo.


Chaka chakhumi ndi chinai ndipo anadza Kedorilaomere ndi mafumu amene anali naye, nawakantha Arefaimu mu Asiteroti-Karanaimu, ndi Azuzimu mu Hamu, ndi Aemimu mu Savekiriyataimu,


Akeni ndi Akenizi, Akadimoni,


ndi Aamori, ndi Akanani, ndi Agirigasi, ndi Ayebusi.


Ndipo Abrahamu anauka pa wakufa wake, nanena kwa ana a Hiti, nati,


Ndipo padzakhala ngati wamasika alikumweta tirigu wosacheka, ndi dzanja lake lilikudula ngala; inde padzakhala ngati pamene wina akunkha ngala m'chigwa cha Refaimu.


Aamaleke akhala m'dziko la kumwera; ndi Ahiti, ndi Ayebusi, ndi Aamori, akhala ku mapiri, ndi Akanani akhala kunyanja, ndi m'mphepete mwa Yordani.


koma muwaononge konse Ahiti, ndi Aamori, Akanani, ndi Aperizi, Ahivi ndi Ayebusi; monga Yehova Mulungu wanu anakulamulirani;


Ndipo Yoswa ananena nao, Ngati muli anthu aunyinji, kwerani kuli mitengoko, ndi kudziswera minda m'dziko la Aperizi ndi la Arefaimu; akakucheperani malo kuphiri la Efuremu.