Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 15:11 - Buku Lopatulika

Pamene miimba inatsikira panyama, Abramu anaingitsa iyo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamene miimba inatsikira panyama, Abramu anaingitsa iyo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Miphamba idadzatera kuti idye nyama zimene adaaphazo, koma Abramu adaipirikitsa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene miphamba inabwera kuti itole nyama ija, Abramu anayipirikitsa.

Onani mutuwo



Genesis 15:11
6 Mawu Ofanana  

Ndipo anatenga iye zonse zimenezo, nazidula pakati, naika bandu popenyana ndi linzake: koma mbalame sanazidule.


Ndipo linalinkulowa dzuwa, ndi tulo tatikulu tinamgwera Abramu: ndipo taonani, kuopsa kwa mdima waukulu kunamgwera iye.


Ndinafotokozera ndi milomo yanga maweruzo onse a pakamwa panu.


nuziti, Atero Ambuye Yehova, Chiombankhanga chachikulu ndi mapiko aakulu, ndi maphiphi aatali, odzala nthenga cha mathothomathotho, chinafika ku Lebanoni, nkutenga nsonga ya mkungudza,


Panalinso chiombankhanga china chachikulu, ndi mapiko aakulu, ndi nthenga zambiri; ndipo taona, mpesa uwu unachipindira mizu yake, nuchilunjikitsira zake, kuchokera pookedwa pake, kuti chiuthirire madzi.


Ndipo m'kufesa kwake zina zinagwa m'mbali mwa njira, ndipo zinadza mbalame, nkulusira izo.