Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 11:22 - Buku Lopatulika

Ndipo Serugi anakhala ndi moyo zaka makumi atatu, nabala Nahori:

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Serugi anakhala ndi moyo zaka makumi atatu, nabala Nahori:

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Serugi ali wa zaka 30, adabereka mwana dzina lake Nahori.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene Serugi anali ndi zaka makumi atatu, anabereka Nahori.

Onani mutuwo



Genesis 11:22
3 Mawu Ofanana  

ndipo Reu anakhala ndi moyo zaka mazana awiri kudza zisanu ndi ziwiri, atabala Serugi, nabala ana aamuna ndi aakazi.


ndipo Serugi anakhala ndi moyo zaka mazana awiri, atabala Nahori, nabala ana aamuna ndi aakazi.


Ndipo Yoswa ananena ndi anthu onse, Atero Yehova Mulungu wa Israele, Kale lija makolo anu anakhala tsidya lija la mtsinje, ndiye Tera, atate wa Abrahamu ndi atate wa Nahori; natumikira milungu ina iwowa.