Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 11:21 - Buku Lopatulika

ndipo Reu anakhala ndi moyo zaka mazana awiri kudza zisanu ndi ziwiri, atabala Serugi, nabala ana aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo Reu anakhala ndi moyo zaka mazana awiri kudza zisanu ndi ziwiri, atabala Serugi, nabala ana aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pambuyo pake adakhala ndi moyo zaka zina 207, ndipo adaberekanso ana ena aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atabereka Serugi, Reu anakhala ndi moyo zaka zina 207 ndipo anali ndi ana ena aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo



Genesis 11:21
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Reu anakhala ndi moyo zaka makumi atatu kudza ziwiri, nabala Serugi:


Ndipo Serugi anakhala ndi moyo zaka makumi atatu, nabala Nahori: