Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 11:18 - Buku Lopatulika

Ndipo Pelegi anakhala ndi moyo zaka makumi atatu, nabala Reu;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Pelegi anakhala ndi moyo zaka makumi atatu, nabala Reu;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pelegi ali wa zaka 30 adabereka mwana dzina lake Reu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene Pelegi anali ndi zaka makumi atatu, anabereka Reu.

Onani mutuwo



Genesis 11:18
3 Mawu Ofanana  

ndipo Eberi anakhala ndi moyo zaka mazana anai kudza makumi awiri, atabala Pelegi, nabala ana aamuna ndi aakazi.


ndipo Pelegi anakhala ndi moyo zaka mazana awiri kudza zisanu ndi zinai, atabala Reu, nabala ana aamuna ndi aakazi.


mwana wa Serugi, mwana wa Reu, mwana wa Pelegi, mwana wa Eberi, mwana wa Sela,