Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 11:14 - Buku Lopatulika

Ndipo Sela anakhala ndi moyo zaka makumi atatu, nabala Eberi;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Sela anakhala ndi moyo zaka makumi atatu, nabala Eberi;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene Sela anali wa zaka 30, adabereka mwana dzina lake Eberi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene Sela anali ndi zaka makumi atatu, anabereka Eberi.

Onani mutuwo



Genesis 11:14
2 Mawu Ofanana  

ndipo Aripakisadi anakhala ndi moyo zaka mazana anai kudza zitatu, atabala Sela, nabala ana aamuna ndi aakazi.


ndipo Sela anakhala ndi moyo zaka mazana anai kudza zitatu, atabala Eberi, nabala ana aamuna ndi aakazi.