Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 10:26 - Buku Lopatulika

Ndipo Yokotani anabala Alimodadi, ndi Selefi, ndi Hazara-Maveti, ndi Yera;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yokotani anabala Alimodadi, ndi Selefi, ndi Hazara-Maveti, ndi Yera;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yokotani adabereka Alimodadi, Selefi, Hazara-Maveti, Yera,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yokitani anabereka Alimodadi, Selefi, Hazari-Maveti, Yera,

Onani mutuwo



Genesis 10:26
3 Mawu Ofanana  

Kwa Eberi ndipo kunabadwa ana aamuna awiri; dzina la wina ndi Pelegi; chifukwa kuti m'masiku ake dziko lapansi linagawanikana; dzina la mphwake ndi Yokotani.


ndi Hadoramu ndi Uzali, ndi Dikila;