Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Ezara 2:3 - Buku Lopatulika

ana a Parosi, zikwi ziwiri ndi zana limodzi mphambu makumi asanu ndi awiri kudza awiri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ana a Parosi, zikwi ziwiri ndi zana limodzi mphambu makumi asanu ndi awiri kudza awiri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

A banja la Parosi, 2,172.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Zidzukulu za Parosi 2,172

Onani mutuwo



Ezara 2:3
8 Mawu Ofanana  

Ndi Aisraele a ana a Parosi: Ramiya, ndi Iziya, ndi Matikiya, ndi Miyamini, ndi Eleazara, ndi Malikiya, ndi Benaya.


ndiwo amene adadza ndi Zerubabele, Yesuwa, Nehemiya, Seraya, Reelaya, Mordekai, Bilisani, Misipara, Bigivai, Rehumu, Baana. Kuwerenga kwa amuna a anthu a Israele ndiko:


Ana a Sefatiya, mazana atatu mphambu makumi asanu ndi awiri kudza awiri.


Ndipo akulu a nyumba za makolo ndi awa, ndi chibadwidwe cha iwo okwera nane limodzi kuchokera ku Babiloni, pokhala mfumu Arita-kisereksesi, ndi ichi:


Wa ana a Sekaniya, wa ana a Parosi, Zekariya; ndi pamodzi naye, powawerenga monga mwa chibadwidwe chao, amuna zana limodzi mphambu makumi asanu.


Buni, Azigadi, Bebai,


Palali mwana wa Uzai anakonza pandunji popindirira, ndi nsanja yosomphoka pa nyumba ya mfumu ya kumtunda, imene ili kubwalo la kaidi. Potsatizana naye anakonza Pedaya mwana wa Parosi.


ana a Parosi zikwi ziwiri mphambu zana limodzi kudza makumi asanu ndi awiri.