Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 40:37 - Buku Lopatulika

koma ukapanda kukwera mtambo, samayenda ulendo wao kufikira tsiku loti wakwera.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

koma ukapanda kukwera mtambo, samayenda ulendo wao kufikira tsiku loti wakwera.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma mtambowo ukapanda kuchoka, Aisraele sankachokanso pachigonopo. Ankadikira tsiku lakuti mtambo wachokapo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma ngati mtambo sunachoke, iwo sankasamukanso mpaka tsiku limene udzachoke.

Onani mutuwo



Eksodo 40:37
2 Mawu Ofanana  

Nyengo zanga zili m'manja mwanu, mundilanditse m'manja a adani anga, ndi kwa iwo akundilondola ine.