Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 39:17 - Buku Lopatulika

Ndipo anamanga maunyolo awiri opota agolide pa mphete ziwiri pansonga za chapachifuwa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anamanga maunyolo awiri opota agolide pa mphete ziwiri pa nsonga za chapachifuwa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono zingwe ziŵiri zagolide adazilumikiza ku mphete ziŵiri zija,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anamangirira timaunyolo tiwiri tagolide tija pa mphete za pa ngodya pa chovala chapachifuwacho.

Onani mutuwo



Eksodo 39:17
3 Mawu Ofanana  

ndi maunyolo awiri a golide woona; uwapote ngati zingwe, ntchito yopota; numange maunyolo opotawo pazoikamo.


Anapanganso zoikamo ziwiri zagolide, ndi mphete ziwiri zagolide; naika mphete ziwirizo pansonga ziwiri za chapachifuwa.


Ndi nsonga zake ziwiri zina za maunyolo awiri opotawo anazimanga pa zoikamo ziwiri, nazimanga pa zapamapewa za efodi, m'tsogolo mwake.