Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 38:29 - Buku Lopatulika

Ndi mkuwa wa choperekacho ndiwo matalente makumi asanu ndi awiri, ndi masekeli zikwi ziwiri kudza mazana anai.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi mkuwa wa choperekacho ndiwo matalente makumi asanu ndi awiri, ndi masekeli zikwi ziwiri kudza mazana anai.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mkuŵa umene adaapereka kwa Chauta udakwana makilogaramu 2,425 pamodzi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mkuwa ochokera ku nsembe yoweyula unali makilogalamu 2,425.

Onani mutuwo



Eksodo 38:29
2 Mawu Ofanana  

Ndipo anapanga zokowera za mizati nsanamira ndi nsichi ndi masekeli aja chikwi chimodzi kudza mazana asanu ndi awiri mphambu asanu, nakuta mitu yake, nazigwirizanitsa pamodzi.


Ndipo anapanga nao makamwa a pa khomo la chihema chokomanako, ndi guwa la nsembe lamkuwa, ndi sefa wake amkuwa, ndi zipangizo zonse za guwa la nsembe,