Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 37:27 - Buku Lopatulika

Ndipo analipangira mphete ziwiri zagolide pansi pa mkombero wake, pangodya zake ziwiri, pa mbali zake ziwiri, zikhale zopisamo mphiko kulinyamulira nazo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo analipangira mphete ziwiri zagolide pansi pa mkombero wake, pangodya zake ziwiri, pa mbali zake ziwiri, zikhale zopisamo mphiko kulinyamulira nazo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adapanga mphete ziŵiri zagolide zonyamulira guwalo, ndipo adazilumikiza ku mbali zonse ziŵiri za guwa, pansi pa mkombero uja, kuti apisemo mphiko zonyamulira.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anapanga mphete ziwiri pansi pa mkomberowo ndi kulumikiza ku mbali zonse ziwiri kuti apisemo nsichi zonyamulira.

Onani mutuwo



Eksodo 37:27
3 Mawu Ofanana  

Mphetezo zikhale pafupi pa mitanda, zikhale zopisamo mphiko za kunyamulira nazo gome.


Ndipo analikuta ndi golide woona, pamwamba pake, ndi mbali zake pozungulira, ndi nyanga zake; ndipo analipangira mkombero wagolide pozungulira pake.


Ndipo anazipanga mphiko za mtengo wakasiya, nazikuta ndi golide.