Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 37:24 - Buku Lopatulika

Anachipanga ichi ndi zipangizo zake zonse za talente wa golide woona.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Anachipanga ichi ndi zipangizo zake zonse za talente wa golide woona.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Popanga choikaponyalecho, pamodzi ndi zipangizo zake zonsezo, adagwiritsa ntchito makilogaramu 34 a golide wabwino kwambiri.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iwo anapanga choyikapo nyale ndi zipangizo zake zonse zagolide wabwino kwambiri wolemera makilogalamu 34.

Onani mutuwo



Eksodo 37:24
2 Mawu Ofanana  

Ndipo anapanga nyali zake zisanu ndi ziwiri ndi mbano zake, ndi zoolera zake, za golide woona.


Ndipo anapanga guwa la nsembe lofukizapo la mtengo wakasiya; utali wake mkono, ndi kupingasa kwake mkono, laphwamphwa; ndi msinkhu wake mikono iwiri; nyanga zake zinatuluka m'mwemo.