Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 37:18 - Buku Lopatulika

ndi m'mbali zake munatuluka mphanda zisanu ndi imodzi; mphanda zitatu za choikaponyali zotuluka m'mbali yake imodzi, ndi mphanda zitatu za choikaponyali zotuluka m'mbali yake ina;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi m'mbali zake munatuluka mphanda zisanu ndi imodzi; mphanda zitatu za choikapo nyali zotuluka m'mbali yake imodzi, ndi mphanda zitatu za choikapo nyali zotuluka m'mbali yake ina;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pa mbali zake adapanga nthambi zisanu ndi imodzi, zitatu pa mbali iliyonse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mʼmbali mwake munali mphanda zisanu ndi imodzi, zitatu mbali iliyonse.

Onani mutuwo



Eksodo 37:18
4 Mawu Ofanana  

ndipo m'mbali zake mutuluke mphanda zisanu ndi imodzi; mphanda zitatu za choikaponyalicho zituluke m'mbali yake ina, ndi mphanda zitatu za choikaponyalicho zituluke m'mbali inzake.


Ndipo anapanga choikaponyali cha golide woona; mapangidwe ake a choikaponyalicho anachita chosula, tsinde lake ndi thupi lake, zikho zake, mitu yake, ndi maluwa ake zinakhala zochokera m'mwemo;


pa mphanda imodzi panali zikho zitatu zopangika ngati katungurume, mutu ndi duwa; ndi pa mphanda ina zikho zitatu zopangika ngati katungurume, mutu ndi duwa zinatero mphanda zisanu ndi imodzi zotuluka m'choikaponyali.


Nena kwa Aroni, nuti naye, Pamene uyatsa nyalizo, nyali zisanu ndi ziwirizo ziwale pandunji pake pa choikaponyalicho.