Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 37:15 - Buku Lopatulika

Ndipo anapanga mphiko za mtengo wakasiya, nazikuta ndi golide, kunyamulira nazo gomelo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anapanga mphiko za mtengo wakasiya, nazikuta ndi golide, kunyamulira nazo gomelo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adapanga mphiko za matabwa a mtengo wa kasiya, nazikuta ndi golide.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anapanga nsichi zamtengo wa mkesha ndi kuzikuta ndi golide kuti azinyamulira tebulolo.

Onani mutuwo



Eksodo 37:15
3 Mawu Ofanana  

ndi zikopa za nkhosa zamphongo zonyika zofiira, ndi zikopa za akatumbu, ndi mtengo wakasiya;


Mphetezo zinali pafupi pa mitanda, zikhale zopisamo mphiko kunyamulira nazo gomelo.


Anapanganso zipangizo za gomelo, mbale zake, ndi zipande zake, ndi mitsuko yake, ndi zikho zake zakuthira nazo, za golide woona.