Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 36:32 - Buku Lopatulika

ndi mitanda isanu ya matabwa a pa mbali inzake ya chihema, ndi mitanda isanu ya matabwa a chihema ali pa mbali ya kumadzulo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi mitanda isanu ya matabwa a pa mbali inzake ya Kachisi, ndi mitanda isanu ya matabwa a Kachisi ali pa mbali ya kumadzulo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

isanu ya mafulemu a mbali inayo, ndiponso isanu ya mafulemu a mbali yakuzambwe, kumbuyo kwake kwa chihema.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

mitanda isanu inanso inali ya maferemu a mbali inayo ndipo mitanda ina isanu ya mbali yakumadzulo, kumapeto kwenikweni kwa chihema.

Onani mutuwo



Eksodo 36:32
3 Mawu Ofanana  

Ndipo uzipanga mitanda ya mtengo wakasiya; isanu ya matabwa a pa mbali ina ya chihema,


Ndipo anapanga mitanda ya mtengo wakasiya; isanu ya matabwa a pa mbali ina ya chihema,


Ndipo anapititsa mtanda wa pakatipo, pakati pa matabwa kufikira kuthungo.