Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 36:26 - Buku Lopatulika

makamwa awiri pansi pa thabwa limodzi, ndi makamwa awiri pansi pa thabwa lina.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

makamwa awiri pansi pa thabwa limodzi, ndi makamwa awiri pansi pa thabwa lina.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

ndi masinde ake makumi anai asiliva, masinde aŵiri pansi pa fulemu lililonse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ndiponso matsinde makumi anayi asiliva, awiri pansi pa feremu iliyonse.

Onani mutuwo



Eksodo 36:26
2 Mawu Ofanana  

Ndi ku mbali ina ya chihema, mbali ya kumpoto, anapanga matabwa makumi awiri, ndi makamwa ao makumi anai asiliva;


Ndi ku mbali ya kumbuyo ya chihema kumadzulo anapanga matabwa asanu ndi limodzi.