Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 36:25 - Buku Lopatulika

Ndi ku mbali ina ya chihema, mbali ya kumpoto, anapanga matabwa makumi awiri, ndi makamwa ao makumi anai asiliva;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi ku mbali ina ya Kachisi, mbali ya kumpoto, anapanga matabwa makumi awiri, ndi makamwa ao makumi anai asiliva;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pa mbali yakumpoto ya chihemacho adapanganso mafulemu makumi aŵiri

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iwo anapanganso maferemu makumi awiri a mbali yakumpoto ya chihemacho,

Onani mutuwo



Eksodo 36:25
2 Mawu Ofanana  

napanga makamwa makumi anai asiliva pansi pa matabwa makumi awiri; makamwa awiri pansi pa thabwa limodzi kwa mitsukwa yake iwiri, ndi makamwa awiri pansi pa thabwa lina kwa mitsukwa yake iwiri.


makamwa awiri pansi pa thabwa limodzi, ndi makamwa awiri pansi pa thabwa lina.