Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 36:21 - Buku Lopatulika

Utali wake wa thabwa limodzi ndiwo mikono khumi, ndi kupingasa kwake kwa thabwa limodzi ndiko mkono ndi hafu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Utali wake wa thabwa limodzi ndiwo mikono khumi, ndi kupingasa kwake kwa thabwa limodzi ndiko mkono ndi hafu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

M'litali mwa fulemu lililonse munali mamita anai ndi theka, ndipo muufupi mwake munali masentimita 69.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Feremu iliyonse inali yotalika mamita anayi ndipo mulifupi mwake munali masentimita 69.

Onani mutuwo



Eksodo 36:21
2 Mawu Ofanana  

Ndipo anapanga matabwa a chihema, oimirika, a mtengo wakasiya.


Pa thabwa limodzi panakhala mitsukwa iwiri, yomangika pamodzi; anawapanga momwemo matabwa onse a chihema.