Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 35:9 - Buku Lopatulika

ndi miyala yasohamu, ndi miyala yoika ya efodi, ndi ya chapachifuwa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi miyala yasohamu, ndi miyala yoika ya efodi, ndi ya chapachifuwa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

miyala ya mtundu wa onikisi ndi ina yokoma yoika pa chovala chaunsembe cha efodi ndiponso pa chovala chapachifuwa.’ ”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

miyala yokongola ya mtundu wa onikisi ndi ina yabwino yoyika pa Efodi ndi pa chovala cha pachifuwa.

Onani mutuwo



Eksodo 35:9
7 Mawu Ofanana  

ndi zikopa za nkhosa zamphongo zonyika zofiira, ndi zikopa za akatumbu, ndi mtengo wakasiya;


miyala yaberulo, ndi miyala yoika paefodi, ndi pachapachifuwa.


Ndipo utenge miyala iwiri yaberulo, nulochepo maina a ana a Israele;


Ndipo abwere yense wa mtima waluso mwa inu, napange zonse zimene Yehova analamula;


ndi mafuta akuunikira, ndi zonunkhira za mafuta odzoza, ndi chofukiza cha fungo lokoma;