Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 35:10 - Buku Lopatulika

Ndipo abwere yense wa mtima waluso mwa inu, napange zonse zimene Yehova analamula;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo abwere yense wa mtima waluso mwa inu, napange zonse zimene Yehova anauza;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Anthu onse aluso pakati panupa abwere, ndipo apange zonse zimene Chauta adalamula.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Anthu onse aluso pakati panu abwere ndi kupanga zonse zimene Yehova walamula:

Onani mutuwo



Eksodo 35:10
6 Mawu Ofanana  

Ndipo ulankhule ndi onse a mtima waluso, amene ndawadzaza ndi mzimu waluso, kuti amsokere Aroni zovala apatulidwe nazo, andichitire Ine ntchito ya nsembe.


ndi miyala yasohamu, ndi miyala yoika ya efodi, ndi ya chapachifuwa.


Potero anatsiriza ntchito yonse ya Kachisi wa chihema chokomanako; ndipo ana a Israele adachita monga mwa zonse Yehova adamuuza Mose, anachita momwemo.


Ndipo Yehova ananena ndi Mose, ndi kuti,