Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 35:1 - Buku Lopatulika

Ndipo Mose anasonkhanitsa khamu lonse la ana a Israele, nanena nao, Siwa mau amene Yehova analamula, kuti muwachite.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Mose anasonkhanitsa khamu lonse la ana a Israele, nanena nao, Siwa mau amene Yehova anauza, kuti muwachite.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mose adaitana Aisraele onse naŵauza kuti, “Chauta akukulamulani kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mose anasonkhanitsa gulu lonse la Aisraeli ndipo anawawuza kuti, “Zinthu zimene Yehova wakulamulirani kuti muzichite ndi izi:

Onani mutuwo



Eksodo 35:1
7 Mawu Ofanana  

Udzikumbukira tsiku la Sabata, likhale lopatulika.


Ndipo atatero, ana onse a Israele anayandikiza; ndipo iye anawauza zonse Yehova adalankhula naye m'phiri la Sinai.


pakuti akumvaimva lamulo sakhala olungama pamaso pa Mulungu, koma akuchita lamulo adzayesedwa olungama.


Khalani akuchita mau, osati akumva okha, ndi kudzinyenga nokha.