Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 31:9 - Buku Lopatulika

ndi guwa la nsembe yopsereza ndi zipangizo zake zonse, ndi mkhate ndi tsinde lake;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi guwa la nsembe yopsereza ndi zipangizo zake zonse, ndi mkhate ndi tsinde lake;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

guwa la zopereka zopsereza, pamodzi ndi zipangizo zake, beseni losambira ndi phaka lake,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

guwa lansembe yopsereza ndi ziwiya zake zonse, beseni ndi nsichi yake,

Onani mutuwo



Eksodo 31:9
5 Mawu Ofanana  

Guwa la nsembe lomwe lamkuwa, adalipanga Bezalele mwana wa Uri mwana wa Huri linali komweko, ku khomo la chihema cha Yehova; ndipo Solomoni ndi khamulo anafunako.


Udzozenso mkhate ndi tsinde lake, ndi kuupatula.