Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 31:1 - Buku Lopatulika

Ndipo Yehova ananena ndi Mose, ndi kuti,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yehova ananena ndi Mose, ndi kuti,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pambuyo pake Chauta adapitirira kuuza Mose kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo Yehova anati kwa Mose,

Onani mutuwo



Eksodo 31:1
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Mose anasonkhanitsa khamu lonse la ana a Israele, nanena nao, Siwa mau amene Yehova analamula, kuti muwachite.


Ndipo abwere yense wa mtima waluso mwa inu, napange zonse zimene Yehova analamula;


Ndipo Mose anati kwa ana a Israele, Taonani, Yehova anaitana, ndi kumtchula dzina lake, Bezalele, mwana wa Uri, mwana wa Huri, wa fuko la Yuda;


Pamenepo anachita Bezalele ndi Oholiyabu, ndi anthu aluso, amene Yehova adaika luso ndi nzeru m'mtima mwao adziwe machitidwe ake a ntchito yonse ya utumiki wake wa malo opatulika, monga mwa zonse adauza Yehova.


Ndipo Bezalele mwana wa Uri, mwana wa Huri, wa fuko la Yuda, anapanga zonse zimene Yehova adauza Mose.


Ndipo udikiro wao ndiwo likasa, ndi gome, ndi choikaponyali, ndi maguwa a nsembe, ndi zipangizo za malo opatulika zimene achita nazo, ndi nsalu yotchinga, ndi ntchito zake zonse.