Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 30:27 - Buku Lopatulika

ndi guwalo ndi zipangizo zake zonse, ndi choikaponyali ndi zipangizo zake,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi gomelo ndi zipangizo zake zonse, ndi choikapo nyali ndi zipangizo zake,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

tebulo ndi zipangizo zake zonse, choikaponyale pamodzi ndi zida zake, guwa lofukizirapo lubani,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

tebulo, ndi ziwiya zake zonse, choyikapo nyale ndi zipangizo zake, guwa lofukizirapo lubani,

Onani mutuwo



Eksodo 30:27
3 Mawu Ofanana  

Ndipo udzoze nao chihema chokomanako, ndi likasa la mboni,


ndi guwa la nsembe lofukizapo, ndi guwa la nsembe yopsereza ndi zipangizo zake zonse, ndi mkhate wosambiramo ndi tsinde lake.


Kapena sayatsa nyali, ndi kuivundikira m'mbiya, koma aiika iyo pa choikapo chake; ndipo iunikira onse ali m'nyumbamo.