Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 29:16 - Buku Lopatulika

Nuiphe nkhosa yamphongoyo, ndi kutenga mwazi wake, ndi kuuwaza paguwa la nsembe pozungulira.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nuiphe nkhosa yamphongoyo, ndi kutenga mwazi wake, ndi kuuwaza pa guwa la nsembe pozungulira.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono uiphe ndipo utenge magazi ake ndi kuwaza pa mbali zonse za guwa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Uyiphe ndipo utenge magazi ake ndi kuwaza mbali zonse zaguwalo.

Onani mutuwo



Eksodo 29:16
5 Mawu Ofanana  

Utengenso nkhosa yamphongo imodziyo; ndi Aroni ndi ana ake aamuna aike manja ao pamutu pa nkhosa yamphongoyo.


Ndipo upadzule nkhosa yamphongo m'ziwalo zake, ndi kutsuka matumbo ake, ndi miyendo yake, ndi kuziika pa ziwalo zake, ndi pamutu pake.


Pamenepo aiphe ng'ombeyo pamaso pa Yehova; ndipo ana a Aroni, ansembewo, abwere nao mwazi, nawaze mwaziwo pozungulira paguwa la nsembe, lokhala pa khoma la chihema chokomanako.


Ndipo aike dzanja lake pamutu wa chopereka chake, ndi kuipha pa chipata cha chihema chokomanako; ndipo ana a Aroni, ansembewo, awaze mwazi wake paguwa la nsembe pozungulira.