Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 28:31 - Buku Lopatulika

Ndipo uombe mwinjiro wa efodi ndi lamadzi lokha.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo uombe mwinjiro wa efodi ndi lamadzi lokha.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Upange mkanjo wa nsalu yobiriŵira, wophimba chovala cha efodi chija.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Uyipangire efodiyo mkanjo wamtundu wa mtambo.

Onani mutuwo



Eksodo 28:31
7 Mawu Ofanana  

Ndipo amange chapachifuwa pa mphete zake ndi mphete za efodi ndi mkuzi wamadzi, kuti chikhale pa mpango wa efodi; ndi kuti chapachifuwa chisamasuke paefodi.


Ndipo polowa mutu pakhale pakati pake; pakhale mkawo pozungulira polowa pake, wa ntchito yoomba, ngati polowa pa malaya otchinjiriza, pangang'ambike.


Ndipo zovala azisoka ndi izi: chapachifuwa ndi efodi, ndi mwinjiro, ndi malaya opikapika, ndi nduwira, ndi mpango; tero apangire Aroni mbale wako ndi ana ake zovala zopatulika, kuti andichitire Ine ntchito ya nsembe.


Pamenepo utenge zovalazo ndi kuveka Aroni malaya am'kati, ndi mwinjiro wa efodi, ndi efodi, ndi chapachifuwa, ndi kummangira m'chuuno ndi mpango wa efodi woluka mwanzeru;


Ndipo anamveka ndi malaya a m'kati, nammanga m'chuuno ndi mpango, namveka ndi mwinjiro, namveka ndi efodi, nammanga m'chuuno ndi mpango wa efodi nammanga nao pathupi pake.


Ndiponso amake akamsokera mwinjiro waung'ono, nabwera nao kwa iye chaka ndi chaka, pakudza pamodzi ndi mwamuna wake kudzapereka nsembe ya pachaka.