Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 26:28 - Buku Lopatulika

Ndi mtanda wa pakati pa matabwa ufikire kuthungo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi mtanda wa pakati pa matabwa ufikire kuthungo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mtanda wa pakati penipeni pa mafulemuwo ugwire mafulemu onse, kuyambira ku mapeto mpaka ku mapeto.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mtanda wapakati pa maferemuwo uchokere pa maferemu a mbali ina mpaka mbali inanso.

Onani mutuwo



Eksodo 26:28
3 Mawu Ofanana  

ndi mitanda isanu ya matabwa a pa mbali ina ya chihema, ndi mitanda isanu ya matabwa a pa mbali ya chihema cha kumbuyo kumadzulo.


Ndipo uzikuta matabwa ndi golide, ndi kupanga mphete zao zagolide zopisamo mitandayo; uzikutanso mitandayo ndi golide.


Ndipo anapititsa mtanda wa pakatipo, pakati pa matabwa kufikira kuthungo.