Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 25:39 - Buku Lopatulika

Achipange ichi ndi zipangizo izi zonse za talente wa golide woona.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Achipange ichi ndi zipangizo izi zonse za talente wa golide woona.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Choikaponyalecho ndi zipangizo zonse uzipange ndi golide wolemera makilogaramu 34.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Choyikapo nyale ndi zipangizo zonse zipangidwe ndi golide wabwino kwambiri wolemera makilogalamu 34.

Onani mutuwo



Eksodo 25:39
2 Mawu Ofanana  

Ndipo mbano zake, ndi zoolera zake, zikhale za golide woona.


Ndipo uyang'anire uzipanga monga mwachifaniziro chao, chimene anakuonetsa m'phirimo.