Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 25:34 - Buku Lopatulika

Ndipo pa choikaponyali chomwe pakhale zikho zinai zopangika ngati katungurume, mitu yake ndi maluwa ake;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pa choikapo nyali chomwe pakhale zikho zinai zopangika ngati katungurume, mitu yake ndi maluwa ake;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pa choikaponyalecho padzakhale maluŵa anai a maonekedwe onga maluŵa amtowo, okhala ndi nkhunje ndi maluŵa ake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pa choyikapo nyalecho pakhale zikho zinayi zopangidwa ngati maluwa amtowo ali ndi mphukira ndi maluwa.

Onani mutuwo



Eksodo 25:34
3 Mawu Ofanana  

Ndipo uzipanga choikaponyali cha golide woona; choikapocho chisulidwe mapangidwe ake, tsinde lake ndi thupi lake; zikho zake, mitu yake, ndi maluwa ake zikhale zochokera m'mwemo;


Ndipo pa choikaponyali chomwe panali zikho zinai zopangika ngati katungurume, mitu yake ndi maluwa ake;


Kapena sayatsa nyali, ndi kuivundikira m'mbiya, koma aiika iyo pa choikapo chake; ndipo iunikira onse ali m'nyumbamo.