Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 25:32 - Buku Lopatulika

ndipo m'mbali zake mutuluke mphanda zisanu ndi imodzi; mphanda zitatu za choikaponyalicho zituluke m'mbali yake ina, ndi mphanda zitatu za choikaponyalicho zituluke m'mbali inzake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo m'mbali zake mutuluke mphanda zisanu ndi imodzi; mphanda zitatu za choikapo nyalicho zituluke m'mbali yake ina, ndi mphanda zitatu za choikapo nyalicho zituluke m'mbali inzake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pa mbali zake pakhale mphanda zisanu ndi imodzi, zitatu pa mbali iliyonse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mʼmbali mwake mukhale mphanda zisanu ndi imodzi, zitatu mbali iliyonse.

Onani mutuwo



Eksodo 25:32
3 Mawu Ofanana  

kulingirira ntchito zaluso, kuchita ndi golide ndi siliva ndi mkuwa,


ndi m'mbali zake munatuluka mphanda zisanu ndi imodzi; mphanda zitatu za choikaponyali zotuluka m'mbali yake imodzi, ndi mphanda zitatu za choikaponyali zotuluka m'mbali yake ina;


Kapena sayatsa nyali, ndi kuivundikira m'mbiya, koma aiika iyo pa choikapo chake; ndipo iunikira onse ali m'nyumbamo.