Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 23:28 - Buku Lopatulika

Ndipo ndidzatumiza mavu akutsogolere amene adzaingitsa Ahivi, Akanani, ndi Ahiti, pamaso pako.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ndidzatumiza mavu akutsogolere amene adzaingitsa Ahivi, Akanani, ndi Ahiti, pamaso pako.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndidzapirikitsa Ahivi, Akanani ndi Ahiti, inu musanafike, ndipo adzathaŵa monga ngati ndaŵatumira mavu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ahivi, Akanaani ndi Ahiti adzathawa ngati kuti ndawatumizira mavu.

Onani mutuwo



Eksodo 23:28
7 Mawu Ofanana  

Akeni ndi Akenizi, Akadimoni,


Mudasoseratu pookapo, idagwiritsa mizu yake, ndipo unadzaza dziko.


ndipo ndidzatuma mthenga akutsogolere; ndipo ndidzapirikitsa Akanani, ndi Aamori, ndi Ahiti, ndi Aperizi, Ahivi, ndi Ayebusi;


Dzisungire chimene Ine ndikuuza lero lino: taona, ndiingitsa pamaso pako Aamori ndi Akanani, ndi Ahiti ndi Aperizi, ndi Ahivi, ndi Ayebusi.


Mulungu wamuyaya ndiye mokhaliramo mwako; ndi pansipo pali manja osatha. Ndipo aingitsa mdani pamaso pako, nati, Ononga.


Komanso Yehova Mulungu wanu adzatumiza mavu pakati pao, kufikira ataonongeka otsalawo, ndi akubisala pamaso panu.