Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 16:27 - Buku Lopatulika

Ndipo kunali tsiku la Sabata, kuti anthu ena anatuluka kukaola, koma sanaupeze.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo kunali tsiku la Sabata, kuti anthu ena anatuluka kukaola, koma sanaupeze.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pa tsiku lachisanu ndi chiŵirilo anthu ena adaapita kuti akatole chakudya, koma sadachipeze.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Komabe anthu ena anapita kuti akatole chakudya tsiku lachisanu ndi chiwiri, koma sanapeze kanthu.

Onani mutuwo



Eksodo 16:27
3 Mawu Ofanana  

Muziola uwu masiku asanu ndi limodzi; koma tsiku lachisanu ndi chiwiri ndilo la Sabata, pamenepo padzakhala palibe.


Ndipo Yehova anati kwa Mose, Mukana kusunga zouza zanga ndi malamulo anga kufikira liti?


Waulesi salima chifukwa cha chisanu; adzapemphapempha m'masika osalandira kanthu.