Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 16:17 - Buku Lopatulika

Ndipo ana a Israele anatero, naola wina wambiri, wina pang'ono.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ana a Israele anatero, naola wina wambiri, wina pang'ono.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Aisraele adachitadi zimenezo. Ena adatola tambiri, koma ena pang'ono.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Aisraeli anachita zonse anawawuza. Ena anatola zambiri ena zochepa.

Onani mutuwo



Eksodo 16:17
2 Mawu Ofanana  

Amenewo ndiwo mau walamulira Yehova, Aoleko yense monga mwa njala yake; munthu mmodzi omeri limodzi, monga momwe muli, yense atengere iwo m'hema mwake.


Ndipo pamene anayesa ndi omeri, iye amene adaola wambiri sunamtsalire, ndi iye amene adaola pang'ono sunamsowe; yense anaola monga mwa njala yake.