Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Amosi 3:4 - Buku Lopatulika

Kodi mkango udzabangula m'nkhalango wosakhala nayo nyama? Kodi msona wa mkango udzalira m'ngaka mwake usanagwire kanthu?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Kodi mkango udzabangula m'nkhalango wosakhala nayo nyama? Kodi msona wa mkango udzalira m'ngaka mwake usanagwire kanthu?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kodi mkango umabangula m'nkhalango, usanagwire nyama? Kodi msona wa mkango umakhuluma m'phanga mwake, usanagwire kanthu?

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kodi mkango umabangula mʼnkhalango usanagwire nyama? Kodi msona wamkango umalira mʼphanga mwake pamene sunagwire kanthu?

Onani mutuwo



Amosi 3:4
7 Mawu Ofanana  

Misona ya mkango ibangula potsata nyama yao, nifuna chakudya chao kwa Mulungu.


Adzatsata Yehova, Iye adzabangula ngati mkango; pamene abangula, ana adzafika ndi kunjenjemera kuchokera kumadzulo.


Pakuti ndidzakhala kwa Efuremu ngati mkango, ndi kwa nyumba ya Yuda ngati msona wa mkango; ndidzamwetula Ine ndi kuchoka; ndidzanyamula, ndipo palibe wakulanditsa.


Ndipo anati, Yehova adzadzuma ali mu Ziyoni, nadzamveketsa mau ake ali mu Yerusalemu; podyetsa abusa padzachita chisoni, ndi mutu wa Karimele udzauma.


Kodi awiri adzayenda pamodzi asanapanganiranetu?


Kodi mbalame idzakodwa mumsampha pansi popanda msampha woitchera? Kodi msampha ufwamphuka pansi wosakola kanthu?


Mkango ukabangula, ndani amene saopa? Ambuye Yehova wanena, ndani amene sanenera?