Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Akolose 4:14 - Buku Lopatulika

Akupatsani moni Luka sing'anga wokondedwa, ndi Dema.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Akupatsani moni Luka sing'anga wokondedwa, ndi Dema.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Luka, sing'anga wathu wokondedwa, ndiponso Dema, onsewo akuti moni.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Luka, dotolo wathu wokondedwa ndi Dema, akupereka moni.

Onani mutuwo



Akolose 4:14
3 Mawu Ofanana  

Ndipo m'mene Yesu anamva anati, Olimba safuna sing'anga ai, koma odwala.


ateronso, Marko, Aristariko, Dema, Luka, antchito anzanga.