Akupatsani moni Luka sing'anga wokondedwa, ndi Dema.
Luka, sing'anga wathu wokondedwa, ndiponso Dema, onsewo akuti moni.
Luka, dotolo wathu wokondedwa ndi Dema, akupereka moni.
Ndipo m'mene Yesu anamva anati, Olimba safuna sing'anga ai, koma odwala.
ateronso, Marko, Aristariko, Dema, Luka, antchito anzanga.