Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Akolose 3:6 - Buku Lopatulika

chifukwa cha izi zomwe ukudza mkwiyo wa Mulungu pa ana a kusamvera;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

chifukwa cha izi zomwe ukudza mkwiyo wa Mulungu pa ana a kusamvera;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chifukwa cha zinthu zotere Mulungu amaŵakwiyira anthu osamumvera.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Chifukwa cha zimenezi, mkwiyo wa Mulungu ukubwera pa ana osamvera.

Onani mutuwo



Akolose 3:6
8 Mawu Ofanana  

Ndiye yani mudzikondweretsa momseka? Ndani mulikumyasamira kukamwa, ndi kumtulutsira lilime? Kodi inu simuli ana akulakwa, mbeu yonama?


Pakuti mkwiyo wa Mulungu, wochokera Kumwamba, uonekera pa chisapembedzo chonse ndi chosalungama cha anthu, amene akanikiza pansi choonadi m'chosalungama chao;


Asakunyengeni inu munthu ndi mau opanda pake, pakuti chifukwa cha izi umadza mkwiyo wa Mulungu pa ana a kusamvera.


monga ana omvera osadzifanizitsanso ndi zilakolako zakale, pokhala osadziwa inu;


okhala nao maso odzala ndi chigololo, osakhoza kuleka uchimo, kunyengerera iwo a moyo wosakhazikika; okhala nao mtima wozolowera kusirira; ana a temberero;


Kunja kuli agalu ndi anyanga, ndi achigololo, ndi ambanda, ndi opembedza mafano, ndi yense wakukonda bodza ndi kulichita.