Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Akolose 3:21 - Buku Lopatulika

Atate inu, musaputa ana anu, kuti angataye mtima.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Atate inu, musaputa ana anu, kuti angataye mtima.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu atate, musamaŵapsetsa mtima ana anu, kuti angataye mtima.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Inu abambo, musakwiyitse ana anu, kuti angataye mtima.

Onani mutuwo



Akolose 3:21
7 Mawu Ofanana  

Monga atate achitira ana ake chifundo, Yehova achitira chifundo iwo akumuopa Iye.


pakuti Yehova adzudzula omwe awakonda; monga atate mwana amene akondwera naye.


Ndipo atate inu, musakwiyitse ana anu; komatu muwalere iwo m'maleredwe ndi chilangizo cha Ambuye.


Akapolo inu, mverani m'zonse iwo amene ali ambuye monga mwa thupi, wosati ukapolo wa pamaso, monga okondweretsa anthu, komatu ndi mtima wakulinga kumodzi, akuopa Ambuye;


monga mudziwa kuti tinachitira yense wa inu pa yekha, monga atate achitira ana ake a iye yekha,