Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Akolose 2:21 - Buku Lopatulika

usaikapo dzanja, usalawa, usakhudza,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

usaikapo dzanja, usalawa, usakhudza,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Usagwire chakuti”, “Usakhudze chakuti”?

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Usagwire chakuti,” “Usalawe chakuti,” “Usakhudze chakuti?”

Onani mutuwo



Akolose 2:21
6 Mawu Ofanana  

Koma zipatso za mtengo umene uli m'kati mwa munda, Mulungu anati, Musadye umenewo, musakhudze umenewo, mungadzafe.


Chokani inu, chokani inu, tulukani ku Babiloni; musakhudze kanthu kodetsa; tulukani pakati pake, khalani okonzeka, inu amene munyamula zotengera za Yehova.


Chifukwa chake, Tulukani pakati pao, ndipo patukani, ati Ambuye, Ndipo musakhudza kanthu kosakonzeka; ndipo Ine ndidzalandira inu,


Ngati munafa pamodzi ndi Khristu kusiyana nazo zoyamba za dziko lapansi, mugonjeranji kuzoikikazo, monga ngati moyo wanu mukhala nao m'dziko lapansi,


(ndizo zonse zakuonongedwa pochita nazo), monga mwa malangizo ndi maphunziro a anthu?


a kuletsa ukwati, osiyitsa zakudya zakuti, zimene Mulungu anazilenga kuti achikhulupiriro ndi ozindikira choonadi azilandire ndi chiyamiko.