Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Ahebri 7:23 - Buku Lopatulika

Ndipo iwo ndiwo ambiri anakhala ansembe, popeza imfa idawaletsa asakhalebe;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo iwo ndiwo ambiri anakhala ansembe, popeza imfa idawaletsa asakhalebe;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kusiyana kwina nkwakuti ansembe akale aja anali ambiri, chifukwa ankafa, sankatha kupitirira ndi udindo waowo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsono ansembe akale aja analipo ambiri, popeza imfa imawalepheretsa kupitiriza ntchitoyi.

Onani mutuwo



Ahebri 7:23
7 Mawu Ofanana  

Koma Yohane anati amkanize, nanena, Ndiyenera ine kubatizidwa ndi Inu, ndipo Inu mudza kwa ine kodi?


koma Iye ndi lumbiro mwa Iye amene anenana kwa Iye, Walumbira Ambuye ndipo sadzalapa, iwe ndiwe wansembe nthawi yosatha).


Momwemonso Yesu wakhala Nkhoswe ya pangano loposa.


koma Iye chifukwa kuti akhala Iye nthawi yosatha ali nao unsembe wosasinthika,


Ndipo pano anthu ofeka alandira limodzi la magawo khumi; koma apo iye, woti adamchitira umboni kuti ali ndi moyo.