Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Ahebri 7:20 - Buku Lopatulika

Ndipo monga momwe sikudachitike kopanda lumbiro; (pakuti iwotu anayesedwa ansembe kopanda lumbiro;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo monga momwe sikudachitika kopanda lumbiro; (pakuti iwotu anayesedwa ansembe kopanda lumbiro;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chinanso nchakuti Mulungu adaachita kulumbira. Amene ankaloŵa unsembe kale lija ankatenga udindo waowo popanda lumbiro.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Izi sizinachitiketu wopanda lumbiro. Ena ankakhala ansembe popanda lumbiro.

Onani mutuwo



Ahebri 7:20
5 Mawu Ofanana  

Yehova walumbira, ndipo sadzasintha, Inu ndinu wansembe kosatha monga mwa chilongosoko cha Melkizedeki.


Ndipo iwe ndi ana ako aamuna pamodzi ndi iwe muchite ntchito yanu ya nsembe, pa zonse za ku guwa la nsembe, ndi za m'kati mwa nsalu yotchinga; ndipo mutumikire; ndikupatsani ntchito yanu ya nsembe, utumiki wopatsika kwaulere; koma mlendo wakuyandikiza amuphe.


Monga anenanso mwina, Iwe ndiwe wansembe wa nthawi zonse monga mwa dongosolo la Melkizedeki.


(pakuti chilamulo sichinachitire kanthu kakhale kopanda chilema), ndipo kulinso kulowa nacho chiyembekezo choposa, chimene tiyandikira nacho kwa Mulungu.


koma Iye ndi lumbiro mwa Iye amene anenana kwa Iye, Walumbira Ambuye ndipo sadzalapa, iwe ndiwe wansembe nthawi yosatha).