Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Ahebri 7:12 - Buku Lopatulika

Pakuti posandulika unsembe, kufunikanso kuti lamulo lisandulike.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti posandulika unsembe, kufunikanso kuti lamulo lisandulike.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pakuti pakakhala kusintha pa unsembe, ndiye kuti pa Malamulonso sipangalephere kukhala kusintha.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pakuti pamene unsembe usintha, malamulonso amayenera kusintha.

Onani mutuwo



Ahebri 7:12
7 Mawu Ofanana  

Ndipo ena a iwo ndidzawatenga akhale ansembe ndi Alevi, ati Yehova.


Pamenepo udzakumbukira njira zako ndi kuchita manyazi, pakulandira abale ako aakulu ndi aang'ono; ndipo ndidzakupatsa awa akhale ana ako aakazi, angakhale sali a pangano lako.


Ndipo pakadakhala ungwiro mwa unsembe wa Chilevi (pakuti momwemo anthu analandira chilamulo), pakadatsala kusowa kotani kuti auke wansembe wina monga mwa dongosolo la Melkizedeki, wosayesedwa monga mwa dongosolo la Aroni?


Pakuti Iye amene izi zineneka za Iye, akhala wa fuko lina, wa ili palibe munthu watumikira guwa la nsembe.


Popeza akhala zoikika za thupi zokha (ndi zakudya, ndi zakumwa, ndi masambidwe osiyanasiyana), oikidwa kufikira nthawi yakukonzanso.