Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Ahebri 4:5 - Buku Lopatulika

Ndipo m'menemonso, Ngati adzalowa mpumulo wanga.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo m'menemonso, Ngati adzalowa mpumulo wanga.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Panonso akunena za zomwezo pamene akuti, “Sadzaloŵa konse mu mpumulo umene ndidaŵakonzera.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pa ndime inonso akunena za zomwezo pamene akuti, “Iwo sadzalowa konse mu mpumulo wanga.”

Onani mutuwo



Ahebri 4:5
3 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake ndinalumbira mu mkwiyo wanga, ngati adzalowa mpumulo wanga.


Monga ndinalumbira mu ukali wanga: Ngati adzalowa mpumulo wanga!


Popeza ife amene takhulupirira tilowa mpumulowo, monga momwe ananena, Monga ndalumbira mu mkwiyo wanga, ngati adzalowa mpumulo wanga. Zingakhale ntchitozo zidatsirizika kuyambira kuzika kwa dziko lapansi.