Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Ahebri 2:5 - Buku Lopatulika

Pakuti sanagonjetsere angelo dziko lilinkudza limene tinenali.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti sanagonjetsera angelo dziko lilinkudza limene tinenali.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tikamanena za dziko limene lilikudza, si angelo amene Mulungu adaŵapatsa ulamuliro pa dzikolo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mulungu sanapereke kwa angelo ulamuliro wa dziko limene likubwerali, limene ife tikulinena.

Onani mutuwo



Ahebri 2:5
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Uthenga uwu Wabwino wa Ufumu udzalalikidwa padziko lonse lapansi, ukhale mboni kwa anthu a mitundu yonse; ndipo pomwepo chidzafika chimaliziro.


Pakuti pano tilibe mzinda wokhalitsa, komatu tifunafuna ulinkudzawo.


nalawa mau okoma a Mulungu, ndi mphamvu ya nthawi ilinkudza,


Koma monga mwa lonjezano lake tiyembekezera miyamba yatsopano, ndi dziko latsopano m'menemo mukhalitsa chilungamo.


Ndipo mngelo wachisanu ndi chiwiri anaomba lipenga, ndipo panakhala mau aakulu mu Mwamba, ndi kunena, Ufumu wa dziko lapansi wayamba kukhala wa Ambuye wathu, ndi wa Khristu wake: ndipo adzachita ufumu kufikira nthawi za nthawi.