Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Ahebri 13:19 - Buku Lopatulika

Ndipo ndikudandaulirani koposa kuchita ichi, kuti kubwera kwanga kwa inu kufulumidwe.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ndikudandaulirani koposa kuchita ichi, kuti kubwera kwanga kwa inu kufulumidwe.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndikukupemphani makamaka kuti mupemphere kuti Mulungu andibwezere kwa inu msanga.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ine ndikukupemphani kuti mundipempherere kuti Mulungu andibwezere kwa inu msanga.

Onani mutuwo



Ahebri 13:19
4 Mawu Ofanana  

Koma undikonzerenso pogona; pakuti ndiyembekeza kuti mwa mapemphero anu ndidzapatsidwa kwa inu.


Koma ndidandaulira inu, abale, lolani mau a chidandauliro; pakutinso ndalembera inu mwachidule.