Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Ahebri 12:8 - Buku Lopatulika

Koma ngati mukhala opanda chilango, chimene onse adalawako, pamenepo muli am'thengo, si ana ai.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma ngati mukhala opanda chilango, chimene onse adalawako, pamenepo muli am'thengo, si ana ai.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ngati Mulungu sakulangani inuyo, monga amachitira ndi ana ake onse, ndiye kuti sindinu ana enieni, koma am'chigololo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ngati inu simulangidwa, komatu aliyense amalangidwa, ndiye kuti sindinu ana enieni koma amʼchigololo.

Onani mutuwo



Ahebri 12:8
5 Mawu Ofanana  

Indedi Mulungu achitira Israele zabwino, iwo a mtima wa mbee.


Koma poweruzidwa, tilangidwa ndi Ambuye, kuti tingatsutsidwe pamodzi ndi dziko lapansi.


pakuti iye amene Ambuye amkonda amlanga, nakwapula mwana aliyense amlandira.