Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Ahebri 10:6 - Buku Lopatulika

Nsembe zopsereza zamphumphu ndi za kwa machimo simunakondwere nazo;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nsembe zopsereza zamphumphu ndi za kwa machimo simunakondwera nazo;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nsembe zoocha kwathunthu ndi nsembe zoperekera machimo, simudakondwere nazo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Simunakondwere nazo nsembe zopsereza ndi nsembe zopereka chifukwa cha tchimo.

Onani mutuwo



Ahebri 10:6
9 Mawu Ofanana  

Yehova akondwera nao akumuopa Iye, iwo akuyembekeza chifundo chake.


Nsembe ndi chopereka simukondwera nazo; mwanditsegula makutu. Nsembe yopsereza ndi yamachimo simunapemphe.


Mwenzi atakhala wina mwa inu wakutseka pamakomo, kuti musasonkhe moto chabe paguwa langa la nsembe! Sindikondwera nanu, ati Yehova wa makamu, ndipo sindidzalandira chopereka m'dzanja lanu.


ndipo onani, mau akuchokera kumiyamba akuti, Uyu ndiye mwana wanga wokondedwa, mwa Iyeyu ndikondwera.


ndipo yendani m'chikondi monganso Khristu anakukondani inu, nadzipereka yekha m'malo mwathu, chopereka ndi nsembe kwa Mulungu, ikhale fungo lonunkhira bwino.


Koma ndili nazo zonse, ndipo ndisefukira; ndadzazidwa, popeza ndalandira kwa Epafrodito zija zidachokera kwanu, mnunkho wa fungo labwino, nsembe yolandirika, yokondweretsa Mulungu.


Pakuti sikutheka kuti mwazi wa ng'ombe zamphongo, ndi mbuzi ukachotsera machimo.


Ndipo Samuele anati, Kodi Yehova akondwera ndi nsembe zopsereza ndi nsembe zophera, monga ndi kumvera mau a Yehova? Taonani, kumvera ndiko kokoma koposa nsembe, kutchera khutu koposa mafuta a nkhosa zamphongo.